LAMULO LA MA UKWATI, MABANJA NDI KUTHETSA MAUKWATI
LAMULO LA MA UKWATI, MABANJA NDI KUTHETSA MAUKWATI
Zamkatimu
2. Kodi lamulo limeneli likukhudzana ndi nkhani ngati ziti? 6
3.1. Zoyenereza kuti anthu a kwatirane kapena kulowa m’banja 7
3.2.1 Akazi amene Mwamuna sangakwatile 8
3.2.2 Amuna amene mkazi sangwatiwe nawo 10
3.3 Mitundu ya ma ukwati ku Malawi 11
3.3. 1 Ukwati omangitsidwa ndi mlembi waboma wa za maukwati 11
3.3.1.1 Ndondomeko zoyenera kutsata pomangitsa ukwati omangitsidwa ndi mlembi wa boma wa za ma ukwati 12
3.3.1.2 Ma ukwati omangitsidwa ndi mlembi wa boma wa za ma ukwati motsata chilolezo chapadera 14
3.3.2 Ukwati omangitsa motsata ndondomeko ya mipingo kapena zipempedzo 16
3.3.2.1 Ndondomeko zoyenera kutsata pomanga ukwati wodalitsidwa ku mpingo kapena ku chipembedzo 16
3.3.3 Ukwati omangitsa potsatira miyambo ya makolo kapena chikhalidwe 19
3.3.3.1 Ndondomeko zoyenera kutsata pomanga ukwati otsatira miyambo ya makolo kapena chikhalidwe 19
3.3.4 ..........Ukwati ongolowana popanda kutsatira ndondomeko kapena mwambo uliwonse 22
3.4 Kutsutsa kuti mwamuna ndi mkazi asakwatilane 24
4. Ufulu ndi udindo wa mwamuna ndi mkazi pa banja 25
5. Xxxxxxx ndi zilango zokhudzana ndi ma ukwati 29
6.1 Chisamalilo pa nthawi imene banja lilipo 32
6.2 Chisamalilo pa nthawi imene mlandu wothetsa banja wayambika 34
7. Kuthetsa ukwati ndi Kulekanitsa mwamuna ndi mkazi a pa banja 35
7.1.2 Zoyenera kukwanilitsidwa kuti bwalo la milandu limve pempho lothetsa ukwati 36
7.1.3 Zifukwa zothetsela ukwati 36
7.1.3.1 Umboni osonyeza kuti ukwati wasokonekera ndipo songakonzedwenso 37
7.1.5. Kuthetsa ukwati pachifukwa choganizila kuti mwamuna kapena mkazi anamwalira 39
7.1.6 Zifukwa zimene bwalo limilandu lingakanire kuthetsa ukwati 40
7.2.1 Kugonana mokakamizana pa nthawi ya mlekanitso wa ukwati 43
7.2.2 Katundu opezedwa kapena kugulidwa pa nthawi ya mlekanitso wa ukwati 43
7.3 Kuthetsa ku ukwati pa zifukwa xxxx 44
8.0. Chisamalilo kapena chithandizo pamene ukwati wathetsedwa
8.1 Nyumba yokhala mkazi kapena mwamuna ukwati ukathetsedwa 49
10. Kagawidwe xx xxxxxxx pamene ukwati watha 53
11. Kusokoneza ukwati kwa anthu xxxxx 54
12.0 Udindo opeleka chisamalilo kwa mkazi amene ali ndi pa thupi koma osakwatiwa 56
1. Mawu oyamba
Mchaka cha 2015 boma la Malawi linakhazikitsa lamulo la tsopona loyendetsa maukwati, mabanja ndi kuthetsa kwa ma ukwati.
Lamulo limeneli linalowa m’malo mwa malamulo akale amenne amayendetsa ma banja, ma ukwati, ndikuthetsa ma ukwati. Lamulo latsopanoli linakhazikitsidwa ndi cholinga chothana ndi mavuto osiyanasiyana amene anthu apabanja ndi m’maukwati amakumana nawo. Mwachitsanzo malamulo akale amakondela anthu amuna komanso mbali ina amakondela athu akazi pankhani za ma ufulu ndi ma udindo a pabanja. Komanso malamulo akalewa amapelewela poteteza ma ufulu a wana pamene mabanja athetsedwa.
Cholinga cha lamulo limeneli ndikuwonetsetsa kuti ma ufulu ndi ma udindo a mkazi ndi mwamuna pa banja kapena pa ukwati akutetezedwa mofanana. Motero la mulo limeneli lili ndi mfundo zosiyanasiyana zokhudzana, mwachitsanzo, ndi kalowedwe ka m’banja, kathedzedwe ka ma ukwati, kagawidwe xx xxxxxxx pamene ukwati wathetsedwa kakhalidwe ka pa banja, chithandizo ndi masamalidwe pa banja, kakhalidwe ka mwamuna ndi mkazi
amene anangolowana popanda kutsata ndondomeko ya ukawati ndi xxxx zotero.
Lamulo limeneli likuletsa ma ukwati a mwamuna ndi mkazi amene zaka zawo zakubadwa ndi zochepela 18; likuletsanso kukwatirana anthu amuna okhaokha kapenanso akazi okhaokha; likuletsanso ma ukwati mkazi ndi mwamuna amene ali apachibale cha m’magazi kapena kudzela m’maukwati; likuletsanso ma ukwati okakamizana kapena kuwumilizana komanso likuletsa miyambo ndi zikhalidwe zimene zimapondeleza ma ufulu a mkazi kapena mwamuna pa nkhani za ma ukwati
Pofuna kudziwitsa mtundu wa Malawi za mfundo za lamulo limeneli, buku ili likufotokoza za mfundo zosiyanasiyana za mulalamuloli zimene ndi zofunika kuti anthu azidziwe pa moyo wawo.
2. Kodi lamulo limeneli likukhudzana ndi nkhani ngati ziti? Lamulo limeneli likukhudzana ndi nkhani izi-
(a) Zoyenereza kuti anthu a kwatirane;
(b) Mitundu ya ma ukwati ovomerezedwa ku Malawi
(c) Ndondomeko zoyenera kutsatilidwa pamene mkazi ndi mwamuna akufuna kulowa m’banja kapena kukwatilana;
(d) Anthu oletsedwa kukwatilana ;
(e) Ma ufulu ndi ma udindo a mwamuna ndi mkazi pa banja kapena pa ukwati;
(f) Milandu ndi zilango zokhudzana ndi ma ukwati
(g) Kathetsedwe ka ukwati kapena banja.
(h) Kulekanitsa kwa mkazi ndi mwamuna wa pabanja;
(i) Kagawidwe xx xxxxxxx pamene ukwati kapena banja xxxxx;
(j) Kasamalidwe ka xxx m’ banja
(k) Chithandizo ndi Kasamalidwe ka mkazi ndi mwamuna pa banja komanso pamene banja lathetsedwa.
(l) Chithandizo kwa mkazi osakwatiwa amane ali ndi pathupi;
(m) Kuthana ndi kusokoneza kwa ukwati kapena banja kuchokera kwa a chibale;
(n) Mphamvu za bwalo la Milandu pa nkhani za ma ukwati, mabanja
3.1. Zoyenereza kuti anthu a kwatirane kapena kulowa m’banja
Munthu wa mkazi ndi wa mwamuna amene ali ndi zaka zosachepera 18 zakubadwa komanso amene ubongo wawo umagwira ntchito ndi ovomerezedwa ndi lamulo kukwatilana. Izi zikutanthauza kuti:
(a) Anthu amuna okhaokha kapena akazi okhaokha sangakwatirane
(b) Anthu amene bongo wawo sugwira ntchito sangakwatiwe kapena kukwatira
(c) Anthu amene ali ndi zaka zapakati pa 15 ndi 18 zakubadwa akhoza kulowa m’banja pokhapokha ngati alandira chilolezo kuchokera kwa makolo awo malingani ndi lamulo lalikulu la ku Malawi (Constitution)
Lamulo likuletsa anthu xxx xxxx asakwatilane chifukwa chakuti ndi apachibale chapafupi kudzera m’magazi kapena m’maukwati. Anthu oterewa akakwatirana banja lawo silikhala lovomerezeka ndi lamulo. Motero bwalo la milandu lapatisdwa mphavu zothetsa mabanja amanewa.
Kafukufuku wa zachipatala wasonyeza kuti anthu amene ali pachibale chapafupi cha m’magazi akakwatirana amabereka xxx azilema zosiyanasiyana. Lamulo likuletsanso anthu amane ali pa xxxxx kudzera m’maukwati kuti asakwatilane ndi cholinga chofuna kuthetsa miyambo yosakhala bwino ngati chokolo kapena kulowa kufa.
3.2.1 Akazi amene Mwamuna sangakwatile
Lamulo likuletsa mwamuna kuti asakwatire anthu awa:
(a) Xxxxx xxx omubeleka
(b) Xxxxx xxx omulela
(c) Mwana wake wa mkazi
(d) Mwana wake wa mkazi omupeza kapena omulera
(e) Agogo ake akazi
(f) Mdzukulu wake wamkazi
(g) Mchemwali wake
(h) Azakhali ake
(i) Achemwali a xxxx xxx
(j) Mwana wa mchimwene wake
(k) Mwana wa mchemwali wake
(l) Msuweni wake
(m) Mwana wa mkazi wake xxxxxx
(n) Mkazi xxxxxx wa a bamboo ake
(o) Mkazi xxxxxx wa agogo ake
(p) Mdzukulu wake kuchokera kwa mkazi wake xxxxxx
(q) Amayi a mkazi wake xxxxxx
(r) Mkazi xxxxxx wa mwana wake
(s) Mchemwali wa mkazi wake
(t) Mwana wa mchimwene wa mkazi wake xxxxxx
(u) Mwana wa mchemwali wa mkazi wake xxxxxx
(v) Azakhali a mkazi wake wa kale
(w) A mayi an’gono a mkazi wake
3.2.2 Amuna amene mkazi sangwatiwe nawo
Munthu wa mkazi akuletsedwa kukwatiwa ndi anthu amuna awa:
(a) A bambo ake
(b) Abambo ake omupeza kapena omulera
(c) Mwana wake
(d) Mwana wake omupeza kapena omulera
(e) Agogo ake
(f) Mdzukulu wake
(g) Mchimwene wake
(h) Achimwene a bambo ake
(i) Amalume ake
(j) Mwana wa mchimwene wake
(k) Mwana wa mchemwali wake
(l) Msuweni wake
(m) Mwana wa mwamuna wake xxxxxx
(n) Mwamuna xxxxxx wa xxxxx xxx
(o) Mwamuna xxxxxx wa agogo ake
(p) Mdzukulu wa mwamuna wake xxxxxx
(q) Abambo a mwamuna wake xxxxxx.(Apongozi )
(r) Mwamuna xxxxxx wa mwana wake( Apongozi)
(s) Mchimwene wa mwamuna wake amane anamwalira kapena amene analekana naye banja
(t) Mwana wa mchimwene wa malemu mwamuna wake
(u) Achimwene a bambo wa malemu mwamuna wake
(v) Achimwene a mayi wa malemu mwamuna wake
3.3 Mitundu ya ma ukwati ku Malawi
Lamulo limavomereza mitundu iyi ya ma ukwati kuno ku Malawi:
(a) Ukwati omangitsidwa ndi mlembi waboma wa za maukwati.
(b) Ukwati omangitsidwa motsata ndondomeko za miyambo ndi zikhalidwe za makolo kapena mitundu ya anthu
(c) Ukwati omangitsidwa motsata ndondomeko ya mipingo kapena zipempedzo
(d) Ukwati ongolowana mosatsata ndondomeko ina iliyone
(e) Ukwati omangitsidwa motsata malamulo aku mayiko akunja kwa dziko la Malawi kumene mwamuna kapena mkazi amachokera.
3.3. 1 Ukwati omangitsidwa ndi mlembi waboma wa za maukwati Ukwati umenewu amamanga ndi mlembi wa boma wa za
maukwati kapena munthu amene wapatisidwa mphavu ndi mlembiyi. Padakali pano anthu ovemerezeka ogwila ntchito ku
office ya zakalembela (Registrar General) ndiwo alembi a za maukwati. Ma Office a Registrar General ali mumzinda wa Lilongwe, Blantyre ndi Mzuzu. Chofukinanso kudziwa ndi chakuti bwana mkubwa wa m’boma lililonse (District Commissioner) ali ndi mphavu zomangitsa ma ukwati m’malo mwa mlembi wa boma wa za ma ukwati.
(a) Munthu ofuna kumanga ukwati umenewu akuyenera kusonyeza polemba kwa mlembi wa za ma ukwati kapena a District Commissioner kuti iyeyo ndi osakwatira kapena osakwatiwa.Izi zili choncho chifukwa lamulo limanene kuti munthu amene adzalowe m’banja kapena mu ukwati omangitsidwa ndi mlembi wa za ma ukwati kapena District Commissioner akuyenera kukhala ndi mkazi m’modzi kapena mwamuna m’modzi. Motero, munthu amene walowa mu ukwati oterewu saloledwa ndi lamulo kukhala pa mitala;
(b) Akalemba kusonyeza kuti siokwatira kapena okwatiwa, munthu ofuna kulowa mu ukwatiwu akuyenera kupeleka chidziwitso kwa mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District Commissioner polemba mu mafomu (mapepala) amene amapezeka ku ma ofesiwa mwa ulele. Akatero,
mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District
Commissioner xxxxxxxx xx xxxxxxxxxxx xxx xxxxxxxx mu buku la zidziwitso za ma ukwati(Marriage Notice Book) limene limapezeka mu ma ofesiwa.
(c) Zikatero chidziwitso cha ukwati chidzayikidwa panja pa chitseko cha mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District Commissioner kwa masiku osachepera 21 ndi cholinga choti anthu osiyanasiyana adziwe za ukwatiwu. Izi zimapereka mwayi kapena mpata kwa anthu amene akudziwa zoletsa kuti ukwatiwu usapitilile. Pakatha masiku 21, mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District Commissioner amapereka chilolezo kuti mwamuna ndi mkazi akhoza kukwatilana.
(d ) Chilolezo chikaperekedwa kuti anthu akwatirane, mkazi ndi mwamuna akuyenera kukamangitsa ukwati wawo ku ofesi ya mlembi wa boma wa za maukwati kapena kwa District Commissioner. Ukwati uyenera kumangitsidwa kumaofesiwa zitseko zili zotsekula nthawi ina iliyonse kuyambila 8 koloko m’mawa mpakana 6 koloko madzulo. Izi zikutanthauza kuti ukwati sungamangitsidwe nthawi isanakwane 8 koloko m’mawa komanso nthawi itadutsa 6 koloko madzulo.
(e) Panthawi yomangitsa ukwati payenera kukhala mboni zosachepera ziwili zimene zaka zawo zakubadwa
zikuyenera kukhala zosachepera 18.Mboni zimenezi zikuyeneranso kukhala ndi ubongo ogwila ntchito bwino
(f) Ukwati umayenera kumangitsidwa pasanathe miyezi itatu kuchokera pomwe chidziwitso cha ukwati chinaperekedwa. Ukwati ukamangitsidwa patadutsa miyezi itatuyi, banja lake lidzakhala losavomerezeka ndi lamulo. Mwachoncho, ngati miyezi itatatu yadutsa ukwati usanamangidwe, ofuna kulowa m’banjawo ayenera kutsatanso ndondomeko yonse popelekanso chidziwitso cha ukwati wawo kwa mlembi wa boma wa za maukwati kapena kwa District Commissioner.
(g ) Mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District Commissioner akamangitsa ukwati akuyenera kupeleka setifikate kapena kuti chikalata cha umboni kusonyeza kuti mwamuna ndi mkazi akwatirana. Setifiketi imeneyi ikuyenela kusayinindwa ndi womanga ukwati, mkazi ndi mwamuna amene akukwatilana komanso mboni zosachepera ziwili.
3.3.1.2 Ma ukwati omangitsidwa ndi mlembi wa boma wa za ma ukwati motsata chilolezo chapadera
Lamulo la maukwati llimazindikira kuti pakhoza kukhala zifukwa zapedera zimenene zingapangitse kuti anthu amene akufuna kukwatilana asakwanitse kupeleka chidziwitso chokwana masiku
21 asanakwatirane komanso kukatenga chilolezo chokwatirana kuchokera kwa mlembi wa boma wa za maukwati kapena kwa District Commissioner. Mwachitsanzo mwamuna ndi mkazi amene akufuna kukwatilana mwachangu chifukwa choti onse akupita kudziko la kunja sangakwanitse kudikira masiku 21 a chidziwitso cha xxxxxx xxxxxxxxxxxxxx. Anthu ofuna kukwatilana mwachangu akuyenera kutsata ndondomeko izi:
(a) Choyamba, mwamuna kapena mkazi akuyenera kukapempha Nduna ya boma yoyang’anira za ma ukwati kuti akwatirane posapeleka chidziwitso cha ukwati cha masiku 21.;
(b) Pempho lokapelekedwa kwa Nduna likuyenera kulembedwa ndi kusayinilidwa pa maso pa lawyer, kapena uweluza milandu kapenanso District Commissioner omwenso akuyenera kusayinila kutsimikizila kuti zimene zalembedwa ndi zowona zokhazokha.Pempho xxxxxx kwa Nduna likuyenera kufotokoza mwatsatanetsatane zifukwa zimene zikuyenereza kuti chidziwitso cha ukwati cha masiku 21 chisaperekedwe.
(c) Nduna ikakhutitsidwa ndi zifukwa zimene zaperekedwa, imapereka chilolezo cholemba chapadera kulamula mlembi wa boma wa za maukwati kapena District Commissioner kuti amangitse ukwati posadikira chidziwitso cha ukwati cha masiku 21.
(d) Chilolezo choperekedwa ndi Nduna chikhozanso kulamula mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District Commissioner kuti ukwati umangitsidwe ku xxxx xxx kupatula ku ofesi ya mlembi wa boma wa za maukwati kapena District Commissioner.
3.3.2 Ukwati omangitsa motsata ndondomeko ya mipingo kapena zipempedzo
Ukwati umenewu ndi umene umamangitsidwa kapena kudalitsidwa ndi m’busa kapena mtsogoleri wa chipembedzo kapena mpingo kumene mwamuna kapena mkazi amene akukwatilana amapemphera.
3.3.2.1 Ndondomeko zoyenera kutsata pomanga ukwati wodalitsidwa ku mpingo kapena ku chipembedzo
Anthu ofuna kulowa m’banja lomangitsidwa kapena kudalitsidwa ndi mpingo kapena chipembedzo akuyenera kutsata ndondomeko zoyambilila zimene zimatsatidwa ku mpingo kapena chipembedzo
kumene ukwati udzadalitsidwe. Akatero ndondomeko izi zoyenera kutsatidwa:
(a) Ofuna kulowa m’banja akuyenera kupeleka chidziwitso cha ukwati wawo kwa mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District Commissioner wa m’dela limene ukwati udzachitikire. Chidziwitsochi chimapelekedwa posayina ma fomu amene amapezeka mwa ulele ku ofesi ya mlembi wa za maukwati kapena District Commissioner.
(b) Chidziwitsochi cha ukwati chikalandilidwa chimalembedwa mu buku la zidziwitso za ma ukwati limene limapezeka ku ofesi kwa mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District Commissioner. Chidziwitsochi chimakhomedwanso kwa masiku 21 pa malo awoneka kwagulu la anthu ku ma ofesi a mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District Commissioner ;
(c) Pakatha masiku 21, mlembi wa boma wa za ma ukwati kapena District Commissioner amapereka chilolezo kuti mwamuna ndi mkazi akhoza kukwatilana. Ukwati umayenera kumangitsidwa pasanathe miyezi itatu kuchokera pomwe chidziwitso cha ukwati chinaperekedwa. Ukwati
ukamangitsidwa patadutsa miyezi itatuyi, banja lake lidzakhala losavomerezeka ndi lamulo. Mwachoncho, ngati miyezi itatatu yadutsa ukwati usanamangidwe, ofuna kulowa m’banjawo ayenera kutsatanso ndondomeko yonse popelekanso chidziwitso cha ukwati wawo kwa mlembi wa boma wa za maukwati kapena District Commissioner.
(d) Chilolezo cha ukwati chikapelekedwa, mwamuna ndi mkazi akuyenera kukamangitsa ukwati wawo ku tchalitchi kapena malo a chipempedzo ololedwa ndi boma kuti akhoza Kudalitsa ukwati. Nduna ya boma yoyang’anira ma ukwati ndi imene ili ndi mphamvu yopeleka chilolezo kuti malo a chipembedzo adzidalitsako ukwati. Izi zikutanthauza kuti simalo aliwonse a mpingo kapena chipembedzo amene ali ololedwa kudalitsako ukwati.
(e) Kudalitsa kwa ukwati kukuyenera kutsatira ndondomeko za tchalitchi kapena malo a chipembedzo kumene ukwati ukuchitikira.
(f) Ukwati uyenera kudalitsidwa kapena kumangitsidwa nthawi ina iliyonse kuyambila 8 koloko m’mawa mpakana 6 koloko
madzulo. Panthawi yodalitsa ukwati payenela kukhala mboni zosachepera ziwili ndipo pa anthu odzachitila umboniwo pakuyeneranso kukhala a nkhoswe a anthu amene akulowa m’banja. Mboni za ukwati zikuyenera kukhala ndi zaka zakubadwa zosachepera 18
(g) Ukwati ukadalitsidwa, m’busa kapena mtosogoleri wa chipembedzo akuyenera kupeleka setifiketi ya ukwati imene iyenera kusayinindwa ndi mwamuna ndi mkazi amene akulowa m’banja, odalitsa ukwatiwo ndi mboni ziwili.
3.3.3 Ukwati omangitsa potsatira miyambo ya makolo kapena chikhalidwe
Anthu amene akukwatilana potsatira miyambo ya makolo kapena yachikhaliwe ndi ololedwa kukhala pa banja lamitala. Izi zili motele chifukwa pa zikhalidwe ndi miyambo zosiyanasiyana kuno ku Malawi mitala ndi yololedwa.
3.3.3.1 Ndondomeko zoyenera kutsata pomanga ukwati otsatira miyambo ya makolo kapena chikhalidwe
Anthu amene akufuna kukwatilana potsatira miyambo yamakolo kapena ya chikhalidwe akuyenera poyambilila kutsata ndondomeko za ukwati zimene zimayenerea kutsatidwa pa chikhalidwe kapena molingana ndi miyambo imene anthu asankha. Ndondomeko zimenezi ndi monga mwambo wa
chinkhonswe, mwambo wofunsira mbeta kapenanso kupeleka malowolo. Ndondomeko zachikhalidwe zikatsatidwa anthu ofuna kukwatilana akuyenerano kutsatira ndondomeko izi kuti ukwati wawo uvomerezeke ndi lamulo:
(a) Ofuna kulowa m’banja akuyenera kupeleka chidziwitso cha ukwati wawo kwa mlembi wa boma wa za maukwati kapena District Commissioner wa m’dela limene ukwati udzachitikire. Chidziwitsochi chimapelekedwa posayina ma fomu amene amapezeka mwa ulele ku ofesi ya mlembi wa za maukwati kapena District Commissioner.
(b) Chidziwitsochi chikalandilidwa chimalembedwa mu buku la zidziwitso za ma ukwati limene limapezeka ku ofesi kwa mlembi wa boma wa za maukwati kapena District Commissioner. Chidziwitsochi chimakhomedwanso kwa masiku 21 pa malo awoneka ku gulu la anthu ku ma ofesi a mlembi wa boma wa za maukwati kapena District Commissioner ;
(c) Pakatha masiku 21, mlembi wa boma wa za maukwati kapena District Commissioner amapereka chilolezo kuti mwamuna ndi mkazi akhoza kukwatilana. Ukwati umayenera
kumangitsidwa pasanathe miyezi itatu kuchokera pomwe chidziwitso cha ukwati chinaperekedwa. Ukwati ukamangitsidwa patadutsa miyezi itatuyi, banja lake lidzakhala losavomerezeka ndi lamulo. Mwachoncho, ngati miyezi itatatu yadutsa ukwati usanamangidwe, ofuna kulowa m’banjawo ayenera kutsatanso ndondomeko yonse popelekanso chidziwitso cha ukwati wawo kwa mlembi wa boma wa za maukwati kapena District Commissioner.
(d) Kumanga kwa ukwati kumayenela kutsatira ndondomeko zomwe zimatsatidwa pa chikhalidwe chimene anthu asankha kuti ukwati wawo umangidwile.
(e) Ma ukwati onse amene akumangitsidwa kuyambila pa
3 July 2015 motsatira miyambo ya makolo kapena yachikhalidwe akuyenela kulembetsedwa mu buku la ma ukwati limene limasungidwa ndi mfumu ya yayikulu ya m’dela limene ukwati unamangitsidwira.
(f) Anthu amene akufuna kulowa m’banja potsatila miyambo ya makolo kapena yachikhalidwe alinso ndi ufulu okamangitsa
ukwati wawo kwa mlembi wa boma wa za maukwati kapena District Commissioner xxxxx xxxxxxxxx setifiketi ya ukwati
3.3.4 Ukwati ongolowana popanda kutsatira ndondomeko kapena mwambo uliwonse
Izi zimachitika pamene mwamuna ndi mkazi akukhalira limodzi ngati okwatirana mosatsata ndondomeko ina iliyonse kapena osamangitsanso ukwati mwanjira ina iliyonse. Pofuna kutsimikiza kuti mwamuna ndi mkazi alowa m’banja lotere, lamulo linakhazikhitsa mfundo izi zimene ziyenera kukhutitsidwa ndi bwalo lamilandu:
(a) Mwamuna ndi mkazi akuyenela kukhalira limodzi kwa zaka zosachepera zisanu;
(b) Mwamuna ndi mkazi ayenera kukhalira limodzi ngati anthu okwatirana;
(c) Pakuyenera kukhala umboni osonyeza kuti mwamuna ndi mkazi amagonana ngati anthu a pabanja;
(d) Umboni osonyeza Kudalilana kapena mgwilizano odalilana pa nkhani ya za chuma pakati pa mwamuna ndi mkazi;
awo;
(e) Umwini wa katundu, kagwilitsidwe kakatundu ndi kapezedwe kapena kagulidwe xx xxxxxxx pakati mwamuna ndi mkazi;
(f) Mulingo wa m’mene mwamuna ndi Mkazi atsimikizilana kumakhalira limodzi pa moyo wawo ngati banja;
(g) Kuthandizana kwa mkazi ndi mwamuna posamalila xxx
(h) Mbiri yofala mdela lawo imene imasonyeza kuti anthu a m’delalo amawona mkazi ndi mwamunayo ngati banja kapena anthu okwatilana ; komanso
(i) xxxxx xxxx zosonyeza kuti mwamuna ndi xxxxxxx xxx
pa banja.
Lamulo limavomereza banja longolowana mosatsata ndondomeko ina iliyonse ndi cholinga chofuna kuteteza mwamuna, mkazi komanso xxx obadwa m’banjali makamaka pakakhla mikangano kapena mwamuna ndi mkazi akasiyana, pakagawinidwe xx xxxxx mkazi ndi mwamunayo adakali ndi moyo kapena m’modzi mwa iwo atamwalira komanso kasungidwe ndi kasamalidwe ka xxx. Nthawi zambili izi zikachitika pamakhala anthu omanena kuti mkazi ndi mwamunayo sanali pa banja ndicholinga chakuti mkazi kapena mwamuna asatengepo gawo
pakagawidwe kachuma kapena pakasamalidwe ndi kasungidwe ka xxx.
3.4 Kutsutsa kuti mwamuna ndi mkazi asakwatilane
Munthu amene akudziwa zifukwa zoletsa kuti mkazi ndi mwamuna asakwatilane kapena kuti ukwati wawo usamangidwe ali ndi ufulu odziwitsa mlembi wa boma wa za maukwati kapena a District Commissioner za zifukwazo. Choyenera kuchita ndikukalemba mu buku la ma uthenga a ukwati mawu oti “zoletsedwa” kutsogolo kwa maina a mwamuna ndi mkazi amene akufuna kukwatilanawo.
Munthu amene akutsutsa kuti mwamuna ndi mkazi asakwatilane akuyeneranso kulemba zifukwa zoletsa kuti ukwati usapitile. Munthuyu akuyeneranso kulemba dzina lake ndi adilesi xxxx kapena kumene amakhala. Izi zikatero, mlembi waboma wa za maukwati kapena District Commissioner wa m’dela limene ukwati umayenera kuchitikila akuyenera kutumiza mtsutsowo ku bwalo la milandu.
Bwalo la milandu likalandila za mtsutsowo likuyenera kuchita izi:
(a) Bwalo la milandu likuyenera kuyitansitsa mwamuna ndi mkazi amene akufuna kukwatilana komanso munthu amene akutsutsa kuti ukwati usamagitsidwe ndi cholinga chofuna
kumva mwatsatanetsatane zifukwa zimene zapelekedwa kuti ukwati usamangitsidwe kapena kudalitsidwa.
(b) Bwalo la milandu likakhutitsdwa kuti zifukwa zimene zapelekedwa ndi zosakwanila limafufuta mawu oti “zoletsedwa” amene analembedwa mu buku la ma uthenga a ma ukwati. Bwalo la milandu likuyeneranso kusayinila komanso kusindikiza chidindo cha bwalo la milandu likafufuta mawuwo. Izi zikatero mlembi wa boma wa ma ukwati kapena District Commissioner akuyenera kupeleka chilolezo kwa mkazi ndi mwamuna kuti akhoza kukwatilana.
Chofunika kudziwa ndi chakuti munthu amene wakhumudwa mwanjira ina iliyonse ndi mtsutso kapena chiletso cha ukwati ali ndi ufulu okadandaula ku bwalo la milandu kuti lilamule munthu amene amatsutsa kapena kuletsa za ukwati kuti alipile chindapusa. Izi zili choncho ndi cholinga chofuna kuthana ndi anthu amene amafuna kuyimitsa ukwati popanda zifukwa zogwila mtima
4. Ufulu ndi udindo wa mwamuna ndi mkazi pa banja
Pofuna kuwonetsetsa kuti pasakhale kupondelezana pakati pa mwamuna ndi mkazi pa banja, lamulo linakhazikitsa
mwatsatanetsatane za ma ufulu ndi ma udindo a mwamuna ndi mkazi pa banja motele:
(a) Mkazi ndi mwamuna ali ndi ma ufulu ofanana pa banja
(b) Mwamuna ndi mkazi ali ndi ufulu ofanana okhala limodzi pa nyumba kapena pakhomo la banja lawo. Komanso, mwamuna ndi mkazi ali ndi ufulu ofanana kuti onse adzidziwika ngati anthu okwatilana.
(c) Mkazi ndi mwamuna ali ndi ufulu ofanana ogonana pa banja lawo. Mwamuna kapena mkazi akhoza kukana kugonana pa banja pazifukwa zomveka bwino xxxxx izi:
(i) Pamene umoyo wawo suli bwino chifukwa cha matenda;
(ii) Pamene mkazi wangochila kumene atabereka mwana
(iii) Pamene mwamuna kapena mkazi a kuchila kumene potsatira opaleshoni ya kuchipatala;
(iv) Podela nkhawa kuti kogonana kukhoza kuwononga thupi kapena maganizo a mwamuna kapena mkazi;
(v) Polemekeza miyambo ya makolo
(d) Mwamuna ndi mkazi ali ndi udindo ofanana posunga mwachisinsi ndi modalilana nkhani zimene amakambilana pa banja lawo. Chinsinsi chimenechi chiyenela kusungidwa
ngakhale banja litatha. Mkazi kapena mwamuna akhoza kuwulula nkhani zachinsinsi za pa banja pazifukwa izi-
(i) Pamene umboni wawo ukufunikira pofuna kuwonetsetsa kuti chilungamo chachitika pozenga milandu ya upandu yozengedwa kubwalo la milandu laboma.
(ii) Pozenga milandu yothetsa banja lawo kubwalo la milandu chifukwa pamafunika kupelekedwa umboni wa zinthu zimene amakambilana mwa chinsinsi zimene zingawunikile bwalo lamilandu popeleka chigamulo chake
(e) Mkazi wa pa banja ali ndi ufulu ogwilitsa ntchito dzina la a bambo ake kapena la mwamuna wake panthawi xxxxx xxx pa banja. Akhozanso kugwilitsa dzina la abambo ake ndi la mwamuna wake pamodzi. Mwachitsanzo, ngati xxxxx xx xxxxx wa mkazi ndi Tembo ndipo la mwamuna wake ndi Xxxxx xxxxxxx ali ndi ufulu odziwika ngati Xxxxx Xxxxx kapena Xxxxx Xxxxx kapenanso Xxxxx Xxxxx Xxxxx
(f) Mkazi ali ndi ufulu ogwilitsa dzina la mwamuna wake ngati lake ngakhale banja ndi mwamunayo xxxxx xxxxxx ngakhale mwamuna atamwalira. Mkazi akhoza kuletsedwa kugwilitsa
ntchito dzina la mwamuna wake pokhapokha ngati pali umboni kuti dzinalo akuligwilitsa mwachinyengo kapena mosayenela bwino ;
(g) Mkazi ndi mwamuna ali ndi ufulu osunga um’badwa wake kapena xxxx lake pamene ali pabanja ngakhalenso banja litatha;
(h) Mkazi ndi mwamuna ali ndi udindo othandizana posamalila xxx xxx ndi kuwapatsa zoyenera pa moyo wawo xxxxx zovala, zakudya, malo xxxxx, kuwatengera kuchipatala xxx akadwala ndi kupeleka ndalama zamaphunziro awo kuskukulu.
(i) Mwamuna ndi mkazi ali ndi udindo osamalilana pa zofunika pa moyo wawo wa tsiku ndi tsiku molingana ndi kapezedwe kawo xx xxxxxxx. Chofunika kudziwa ndi chakuti lamulo likuvomeraza kufunikila kwa chisamaliro cha pabanja xxxxx kukonza pa nyumba, kuphika, kuchapa zovala ndi kusamalira xxx pakhomo.
5. Milandu ndi zilango zokhudzana ndi ma ukwati
Lamulo linakhazikitsa milandu ndi zilango zokhudzana ndi kuphwanya kwa malamulo akalowedwe ndi kamangitsidwe ka ma ukwati motele:
(a) Mwamuna wa pa banja lomangitsidwa ndi mlembi wa boma wa ma ukwati kapena District Commissioner sakuyenera ku kwatilanso mkazi wina pamene banja lake lilipo. Mwamunayo akatenga mitala nde kuti wa palamula mlandu. Komanso mkazi wa pa banja lomangitsidwa ndi mlembi wa boma wa ma ukwati kapena District Commissioner sakuyenera ku kwatiwanso pamene banja lake lilipo. Chilango chophwanya lamuloli ndi kulipila chindapusa chokwana K100,000 ndi kukaseweza ku ndende kwa zaka zisanu.
(b) Mwamuna wa pa mphala amene walowa m’banja lomangitsidwa ndi mlembi wa boma wa ma ukwati kapena District Commissioner pamene mwamunayo akudziwa kuti mkazi akumukwatilayo ali pa banja kale nde kuti waphwanya lamulo. Komanso mkazi amene walowa m’banja lomangitsidwa ndi mlembi wa boma wa ma ukwati kapena District Commissioner pamene mkaziyo akudziwa kuti mwamunayo ndi wokwatila kale nde kuti waphwanya lamulo.
Chilango chophwanya lamuloli ndi kulipila chi ndapusa chokwana K100, 000 ndi kukaseweza ku ndende kwa chaka chimodzi.
Milandu imeneyi inakhazikitsidwa chifukwa chakuti mitala siyololedwa kwa munthu amene ali pa banja lomangitsidwa ndi mlembi waboma wa ma ukwati kapena District Commissioner. Banja limeneli ndi la mkazi m’modzi ndi mwamuna m’modzi basi. Munthu amene akufuna kulowa mitala akuyenera kulowa m’banja lomangitsa potsata miyambo ya makolo kapena chikhalidwe kapenanso banja lomangitsidwa ndi mpingo kapena chipembedzo chimene chimavomeleza mitala.
(c) Munthu amene wanena kapena kulemba zonama pankhani za maukwati kwa mlembi waboma wa za maukwati kapena District Commissioner akuyenera kulandila chilango chokaseweza ku ndende kwa chaka chimodzi komanso kulipila chindapusa cha ndalama zokwana K100,000
(d) Munthu amene wapanga kapena kupeleka chiphaso, chilolezo kapena setifiketi yokhudzana ndi ukwati yabodza kapena ya chinyengo akuyenera kulandila chilango
chokaseweza ku ndende kwa chaka chimodzi komanso kulipila chindapusa cha ndalama zokwana K100,000
(e) Mlembi wa boma wa za maukwati, District Commissioner, m’busa kapena mtosogoleri wa chipembedzo amene wadalitsa kapena kumangitsa ukwati akudziwa kuti ndondomeko xxxx za ukwatiwu sizinatsatidwe akuyenera kulandila chilango chokaseweza ku ndende kwa zaka zisanu komanso kulipila chindapusa cha ndalama zokwana K100,000
(f) Munthu amene wamanga kapena kudalitsa ukwati pamene alibe mphavu kapena zomuyenereza kumanga kapena kudalitsa ukwati akuyenera kulandila chilango chokaseweza ku ndende kwa zaka zisanu komanso kulipila chindapusa cha ndalama zokwana K100,000
(g) Munthu wodalitsa kapena kumanga ukwati amene wakanika kapena kulephera kukasiya kwa mlembi wa boma wa ma ukwati chikope cha cha setifiketi ya ukwati imene iye wadalitsa kapena kumanga akuyenera kulandila chilango chokaseweza ku ndende kwa zaka zisanu komanso kulipila chindapusa cha ndalama zokwana K100,000.Izi zili
chomwecho chifukwa chakuti munthu odalitsa kapena kumangitsa ukwati ali ndi udindo wokasiya kwa mlembi wa boma wa ma ukwati chikope cha setifikitei ya ukwati umene iye wadalitsa kapena kumangitsa. Cholinga cha udindowu ndi kuthandiza boma kuti likhale ndi tsatanetsatane wa chiwelengelo cha ma ukwati amene akumangitsidwa kapena kudalitsidwa mdziko xxxx la Malawi.
(h) Munthu amene akunamizira kuti ndi munthu wina wake pomangitsa ukwati komanso munthu amene akukwatila kapena kukwatiwa pogwilitsa xxxxx xx xxxxx ndi cholinga chonamiza munthu amane akukwatilana naye akuyenera kulandila chilango chokaseweza ku ndende kwa zaka zisanu komanso kulipila chindapusa cha ndalama zokwana K100,000
6.1 Chisamalilo pa nthawi imene banja lilipo
(a) Lamulo limapeleka udindo kwa mwamuna ndi mkazi m’banja osamalirana komanso kusamalira xxx xxx popeleka zinthu xxxxx chakudya, zovala, malo xxxxx, maphunzio ndi xxxx zofunika pa moyo wa munthu. Izi zimatchiludwa kuti Chisamalilo cha pa banja
(b) Mkazi ali ndi ufulu okapempha bwalo la milandu kuti lilamule mwamuna wake amane akunyalanyaza kuti apeleke chisamalilo cha pa banja kwa mkaziyo ndi xxx pakhomo. Mwanunanso alinso ndi ufulu okapempha bwalo la milandu kuti lilamule mkazi wake amane akunyalanyaza kuti apeleke chisamalilo cha pa banja kwa mkaziyo ndi xxx a pakhomo.
(c) Xxxxxx xxxxxx a chibale a mwamuna kapena mkazi ali ndi ufulu okapempha m’malo mwamuna kapena mkaziyo kuti mkazi kapena mwamuna amene akunyalanyaza udindo wake wopeleka chisamalilo cha pabanja kuti adzipeleka chisamalilocho. Ufulu umenewu unapelekedwanso kwa makolo ndi a chibale a mwamuna kapena mkazi wa pa banja pofuna kuthandiza mwamuna kapena mkazi wa pa banja amene akukanika pa zifukwa zosiyanasiyana kuti akadandaule payekha kubwalo la milandu pa nkhani zokhudzana ndi chisamalilo cha pa banja
(d) Makolo ndi a chibale alinso ndi udindo okadandaula ku unduna oyan’ganila zakasamalidwe ka anthu ngati akuwona kuti mwamuna kapena mkazi wa pabanja akunyalanyaza kupeleka chisamalilo cha pabanja lake zimene zikupeleke chiwopsezo pa moyo, thanzi, maphunzilo ndi chitetezo xxx xxx, mkazi kapena mwamuna pa banjalo. Unduna
oyan’ganila zakasamalidwe ka anthu uli ndi mphavu zothandizila kuti mwamuna ndi mkazi asiyane kwakanthawi komanso kukapempha bwalo la milandu kuti lilamule mwamuna kapena mkazi kuti apeleke chisamalilo cha pa banja.
(e) Bwalo la milandu linapatsidwa mphavu zolamula mwamuna kapena mkazi kuti adzipeleka chisamalilo cha pa banja ndi cholinga chofuna kuthana ndi azibambo kapena azimayi apabanja amene amathawa kapena kunyalanyaza udindo wawo osamalira ma banja awo.
6.2 Chisamalilo pa nthawi imene mlandu wothetsa banja wayambika
Mwamuna kapena mkazi amene wayambitsa mlandu othetsa banja kapena ofuna kuti alekane kwa ka nthawi ali ndi ufulu opempha bwalo la milandu kuti lilamule mwamuna kapena mkazi kuti adzipeleka chisamalilo chosiyanasiyana kwa mkaziyo kapena mwamunayo pa nthawi imene akudikila kuti mlanduwo xxxx. Chisamalilochi chimatchulidwa kuti “Chisamalilo choyembekezela kuweluza mlandu” ndipo chimathandiza mwamuna kapena mkazi kuti adzilandilabe chisamalilo kuchokera kwa mkazi wake kapena mwamuna wake angakhale ukwati wawo wasokonekera kapena
pamene m’modzi mwa iwo wakadandaula ku bwalo la milandu. Izi zili chomwchi pozindikila kuti milandu imatenga nthawi kuti ithe kuzengedwa ndipo mwamuna kapena mkazi akuyenelabe kusamalidwa mpakana pamene bwalo lamilandu laweluza mlandu.
Polamula mwamuna kapena mkazi kuti adzipeleka chisamalilo choyembekezela kuweluza mlandu, bwalo la milandu limawunika xxxxx xxxxxxx mwamuna ndi mkazi ali nacho komanso xxxxxx xxxx xxxxxx xxxxx lamilandu lingathe kulingalila. Chisamalilochi chimayenela kupelekedwa mpakana pamene bwalo la milandu lagamula kuti ukwati watha.
7. Kuthetsa ukwati ndi Kulekanitsa mwamuna ndi mkazi a pa banja
Bwalo la milandu ndi lokhalo limene lili ndi mphamvu zothetsa ma ukwati mdziko xxxx. Izi zikutanthauza kuti mafumu, ankhoswe, a mpingo kapena makolo alibe mphavu zothetsa ukwati wina uliwonse. Mwamuna kapena mkazi ali ndi ufulu okapempha bwalo la milandu kuti lithetse ukwati wawo pa zifukwa zosiyanasiyana zimene tilongosole kutsogoloku.
7.1.2 Zoyenera kukwanilitsidwa kuti bwalo la milandu limve pempho lothetsa ukwati
Bwalo limilandu lisanayambe kumva mwatsatanetsatane pempho lothetsa ukwati, likuyenera kukhutitsidwa kuti ndi limodzi mwa mfundo izi:
(a) Mwamuna kapena mkazi opempha kuti ukwati wake xxxx akuyenera kusonyeza kuti akukhala ku Malawi mokhazikika pa nthawi imene iye akukapempha bwalo limilandu kuti lithetse ukwatiwo. Izi zikutanthauza kuti munthu okhazikika kunja kwa dziko xxxx xxxxx wangobwela pa tchuthi kapena kwa nthawi kopchepa ku Malawi sakuloledwa kupempha bwalo limilandu ku Malawi kuti lithetse ukwati wake; kapena
(b) Ukwati umene ukufuna kuthetsedwa ukuyenela kuti unamangitsidwa ku Malawi. Izi zikutanthauza kuti munthu amene akukhala kunja kwa dziko xxxx xxx ndi ufulu opempha bwalo la milandu m’dziko xxxx xxxx lithetse ukwati wake ngati ukwatiwo unamangitsidwa m’xxxxx xxxx.
7.1.3 Zifukwa zothetsela ukwati
Kuti ukwati uthetsedwe pakuyenera kukhala umboni osonyeza kuti ukwatiwo wasokonekera ndipo sungakonzekedwenso. Izi
zikutanthauza kuti ukwati sungathetsedwe chifukwa chakuti mwamuna ndi mkazi agwilizana kuthetsa ukwati.
7.1.3.1 Umboni osonyeza kuti ukwati wasokonekera ndipo songakonzedwenso
Pofuna kuti bwalo la milandu likhutitsidwe kuti ukwati wasokonekera ndipo sungakonzedwenso, mkazi kapena mwamuna opempha kuti ukwati uthetsedwe akuyenera kupeleka umboni osonyeza kuti:
(a) Odandaulidwa (mwamuna kapena mkazi) wachita chigololo kapena kuti wapanga za chiwelele ndi munthu wina osati mkazi kapena mwamuna wake;
(b) Mwamuna odandaulidwa wapezaka olakwa ndi bwalo la milandu pa mlandu ogwilila mkazi wina aliyense kuphatikizapo mkazi wake yemwe;
(c) Mkazi kapena mwamuna odandaulidwa wapezaka olakwa ndi bwalo la milandu pa mlandu opanga za chiwelele motsutsana ndi chilengedwe;
(d) Mkazi kapena mwamuna odandaulidwa wapezaka olakwa ndi bwalo la milandu pa mlandu opanga za chiwelewele ndi ziweto kapena nyama za kutchire;
(e) Mkazi kapena mwamuna odandaulidwa wapezaka olakwa ndi bwalo la milandu pa mlandu ololelaza munthu wa mkazi kapena wa mwamuna kuti apange naye za chiwelewele motsutsana ndi chilengedwe;
(f) Mkazi kapena mwamuna odandaulidwa wamusiya odandaula popanda chifukwa kwa nthawi yosachepela chaka pofika nthawi imene odandaulayo wakapempha bwalo la milandu kuti lithetse ukwati wawo;
(g) Mkazi kapena mwamuna odandaulidwa wakhala akudwala matenda a misala kapena ozunguza bongo amene sangachilitisidwe ndipo odwalayo wakhala akulandila chithandizo kwa nthawi yosalekeza kwa zaka ziwili pofika nthawi imene odandaula wakapepmpha kuti ukwati uthetsedwe ku bwalo la milandu;
(h) Mkazi kapena mwamuna odandaulidwa wakhala akumuchitila nkhaza odandaula pa banja lawo kapena ukwati wawo
Bwalo limilandu likhozanso kuwunika kapena kulandila umboni wina uliwonse umene ungalithandize kuti likhutitsidwe kuti banja lasokonekera ndipo silingakonzedwenso
Mkazi kapena mwamuna amene akupempha kuti ukwati wake uthetsedwe chifukwa chakuti odandaulidwa wa chita chigololo akuyenera kupeleka xxxxx xx xxxxxx amene odandaulidwa wachita naye chigololocho. Koma ngati munthuyo anamwalira kapena dzina lake silikudziwika sakuyenela kupeleka dzina lililonse.
Choyenela kudziwa ndi chakuti ngati mwamuna ndi mkazi pa banja apitiliza kumagonana mosakakamizana pamene akudziwa kuti m’modzi mwa iwo wachita chigololo ndiye kuti chigololocho chakhululukidwa. Zikatelo bwalo la milandu silingathetse ukwatiwo chifukwa cha chigololocho.
7.1.5. Kuthetsa ukwati pachifukwa choganizila kuti mwamuna kapena mkazi anamwalira
Mkazi kapena mwamuna akamwalira ndekuti ukwati umene unalipo watha.Zisifunika bwalo la milandu kuti litsimikize kuti ukwati watha. Chofunika kudziwa ndi chakuti ngati mwamuna kapena mkazi wa pa banja wachoka pa banja lake kwa nthawi yosalekeza kukwanira zaka 7( zisanu ndi ziwiri) ndipo
sipakupezeka umboni osonyeza kuti xxx xxxx, bwalo la limilandu linapatsidwa mphavu zothetsa ukwatiwu poyelekeza kuti mkaziyo kapena mwamunayo anamwalira. Mwachitsanzo, ngati mwamuna wachoka pa banja lake kwa zaka 7 ndipo palibe umboni osonyeza kuti adakali moyo, mkazi wake ali ndi ufulu okapempha bwalo limilandu kuti lithetse ukwati wawo chifukwa chakuti mwamuna wake akuyenela kuti anamwalira.
7.1.6 Zifukwa zimene bwalo limilandu lingakanire kuthetsa ukwati Bwalo lamilandu lili ndi ufulu okana kuthetsa ukwati ngakhale pali
umboni osonyeza kuti ukwati wasokonekera ndipo songakonzedwenso. Bwalo lamilandu likhoza kutero pa zifukwa izi:
(a) Mkazi kapena mwamuna amene akupempha kuti ukwati xxxx anachitapo chigololo;
(b) Mkazi kapena mwamuna amene akupempha kuti ukwati xxxx watenga nthawi yayitali popanda zifukwa zokwanila asanakapemphe bwalo lamilandu kuti lithetse ukwati;
(c) Mkazi kapena mwamuna amene akupempha kuti ukwati xxxx ndi amene amachitila nkhanza kwa mzake;
(d) Mkazi kapena mwamuna amene akupempha kuti ukwati xxxx ndi amene anayamba kuchoka kapena kuthawa
pa banja lake mzake asanachite chigololo kapena nkhanza zimene zapangitsa kuti akapemphe kuti ukwati xxxx;
(e) Ngati kunyalanyaza kapena khalidwe la Mkazi kapena la mwamuna amene akupempha kuti ukwati xxxx ndi zimene zapangitsa kuti mzake achite chigololo, kapena apange misala kapena kusokonekera bongo, kapena kuthawa pa banja ;
(f) Zochita xxxx xxxx zonse kapena kulephere kuchita zili zonse zimene zachokera kwa mwamuna kapena mkazi amene akupempha kuti ukwati xxxx zomwe zapangitsa kuti ukwati usokonekere.
Izi zikutanthauza kuti mkazi kapena mwamuna amene akupempha kuti ukwati wake uthetsedwe akuyenela kuwonetsetsa kuti sanathandizire kapena kutengapo gawo pakachitikidwe ka zifukwa zimene zapangitsa kuti ukwati wake usokonekere. Ngati pali umboni osonyeza kuti mkazi kapena mwamuna amene akupempha kuti ukwati xxxx ndiye gwelo la zifukwa zimene akufuna kuthetsela ukwatiwo, bwalo lamilandu lidzakana kuthetsa ukwatiwo.
Bwalo lamilandu lili mphavu zolamula kuti mwamuna ndi mkazi asiye kukhalira limodzi kwa kanthawi ngati pali umboni osonyeza
kuti ukwati wawo wasokonekera. Chilamulochi chimadziwika kuti “mlekanitso wa ukwati”. Izi sizitanthauza kuti ukwati watha ayi koma simasonyeza kuti ukwatiwo wayimitsidwa xxxx
Mlekanitso wa ukwati umathandiza mkazi ndi mwamuna kuti akalingalile mozama pa nkhani zimene zikubweletsa mavuto pa ukwati wawo. Mlekanitsowu umathandizanso mkazi kapena mwamuna kuti apeze mpumulo pa ziphinjo zimene akuzipeza ba ukwati wake. Mkazi ndi mwamuna alinso ndi ufulu okapempha bwalo lamilandu kuti lichotse mlekanitso wa ukwati wawo ndi cholinga chakuti ayambenso kukhalila limondzi.Koma ngati mkazi ndi mwamuna akuwona kuti sangathenso kukhalira limodzi, m’modzi mwa iwo akhoza kupempha bwalo lamilandu kuti lithetse ukwatiwo.
Bwalo la milandu likamalamula za mlekanitso wa ukwati likhozanso kulamula kuti:
(a) Katundu wa pa banja wothandiza pa moyo wa mkazi kapena mwamuna agawidwe kwa mwamuna ndi mkaziyo; kapena
(b) Katundu wa pabanja asagawidwe kapena kupelekedwa kwa anthu ena aliwonse pokhapokha ngati pali umboni osonyeza kuti mkazi ndi mwamuna agwilizana
zakagawidwe kapena kupeleka katunduyo kwa anthu ena; komanso
(c) Mkazi kapena mwamuna apeleke ndalama kwa mzake kamodzi kapena pan’gonopang’ono, kapena kuti apeleke katundu ofunikira pa moyo wa mkazi kapena mwamuna ndi xxx. Zofunikirazi ndi xxxxx xxxx, zovala, zakudya ndi chisamalilo cha pa khomo zolingana ndi ndalama zimene bwalo la milandu lingalamule
7.2.1 Kugonana mokakamizana pa nthawi ya mlekanitso wa ukwati
Mwamuna adzazengedwa mlandu ogwilila akagonana ndi mkazi wake mokakamiza pa nthawi ya mlekanitso wa ukwati.
7.2.2 Katundu opezedwa kapena kugulidwa pa nthawi ya mlekanitso wa ukwati
Kuchokera pa nthawi imene mwamuna ndi mkazi akhala pa mlekanitso wa ukwati, lamulo ikufotokoza motele pa nkhani za katundu:
(a) Mwamuna ndi mkazi adzatengedwa ngati si okwatilana pa nthawi ya mlekanitso pokudzana ndi katundu amene mkazi kapena mwamuna angapeze kapena kugula mwa iye
yekha pa nthawi ya mlekanitsowo. Mwachitsanzo, ngati mkazi wagula nyumba payekha pa nthawi xxxxx xxx pa mlekanitso wa ukwati, nyumbayo idzatengedwa kuti ndi ya mkazi pa yekha ngati kuti ndi osakwatiwa. Iye ali ndi ufulu opanga chilichonse ndi nyumbayo.;
(b) Mwamuna kapena mkazi akamwalira osasiya ndondomeko yolemba ya m’mene adzagawile chuma kapena katundu wake (will), katundu yense amene anapeza kapena kugula payekhapayekha pa nthawi ya mlekanitso wa ukwati adzagawidwa ngati kuti mwamuna ndi Mkaziyo anali osakwatirana. Mwachitsanzo, ngati mwamuna wagula nyumba payekha pa nthawi ya mlekanitso wa ukwati ndipo nkumwalira osasiya will, mkazi wake sadzakhala ndi gawo pa nyumbayo
7.3 Kuthetsa ku ukwati pa zifukwa xxxx
Xxxxxx xxxx kuti bwalo lamilandu lili ndi mphamvu zothetsa ukwati ngati pali umboni osonyeza kuti ukwatiwo wasokonekera ndipo sungakozedwenso. Komanso choyenera kudziwa ndi chakuti bwalo la milandu likhozanso kuthetsa ukwati pa zifukwa xxxx zimene lamulo linakhazikitsa. Zifukwa zimenezi
zinakhazikitsidwa pofuna kuwonetsetsa kuti ma ukwati osayenela asapitilile kukhalopo mdziko xxxx.Zifukwazi zili motele:
:
(a) Ngati mwamuna sangathe kugonana ndi mkazi wake chifukwa chakuti umuna wake sutha kugwila ntchito ndipo sungadzuke mkomwe. Choyenera kudziwa ndi chakuti bwalo la milandu silingathetse ukwati chifukwa chakuti mwamuna ndi osabeleka;
(b) Ngati mwamuna ndi mkazi ndi a pachibale chapafupi kudzera m’magazi kapena m’maubale a ukwati;
(c) Ngati mwamuna kapena mkazi anali wamisala pa nthawi imene amakwatirana. Bwalo lamilandu lidzathetsa banjalo pokhapokha ngati pali umboni osonyeza kuti odandaulayo sankadziwa kuti mzakeyo ndi wa misala pa nthawi imene amakwatirana;
(d) Ngati pali umboni osonyeza kuti mwamuna kapena mkazi wake xxxxxx xxxxx ankaganiziridwa kuti anamwalira xxx xxxx;
(e) Ngati pali umboni osonyeza kuti mwamuna kapena mkazi analowa m’banja mokakamizidwa, mowumilizidwa, monamizidwa kapena mwachinyengo;
(f) Ngati mkazi ndi mwamuna sanagonanepo chiloweleni m’banja lawo chifukwa chakuti mkazi kapena mwamuna sakufuna kugonana popanda mfundo ili yonse;
(g) Ngati pali umboni osonyeza kuti mkazi kapena mwamuna amadwala matenda opatsirana pogonana pa nthawi imene amakwatirana ndipo ofuna kuthetsa ukwatiwo sankadziwa kuti mzakeyo ali ndi matenda otelo pa nthawi ya ukwati wawo. Kuwonjezera apo odandaulayo akuyenera kupeleka umboni osonyeza kuti sanapitilize kugonana mwakufuna ndi mwamuna kapena mkazi wake atadziwa za matendawo.
(h) Ngati pali umboni osonyeza kuti pa nthawi ya ukwati, mkazi anali pa thupi ndi munthu wina osati mwamuna wakeyo. Mwamuna ayenela kupeleka umboni ku bwalo lamilandu osonyeza kuti sankadziwa za pathupipo ndipo sanapitilize kugonana ndi mkaziyo atadziwa za pathupipo.
Mwamuna akuyenela kuwonetsetsa kuti wapempha bwalo la milandu kuti lithetse ukwatiwu pasanathe chaka chimodzi chimangileni ukwatiwo.
(i) Ngati pali umboni osonyeza kuti mwamuna anali atapeleka pathupi kwa mkazi wina pa nthawi imene amakwatirana. Mkazi akuyenela kupeleka umboni osonyeza kuti sankadziwa za pathupipo pa nthawi imene amakwatirana ndipo sanapitilize kugonana ndi mwamuna wakeyo atadziwa za nkhaniyi. Mkazi akuyenera kuwonetsetsa kuti wapempha bwalo la milandu kuti lithetse ukwatiwo pasanathe chaka chimodzi chimangileni ukwatiwo.
8.0. Chisamalilo kapena chithandizo pamene ukwati wathetsedwa
(a) Pamene ukwati wathetsedwa, bwalo la milandu lili ndi mphamvu zolamula mkazi kapena mwamuna kuti adzipelekabe chisamalilo kapena chithandizo kwa mzake. Cholinga cha chisamalilochi ndikufuna kuwonetsetsa kuti ngakhale ukwati watha, mkazi kapena mwamuna asavutike pa zosowa za moyo wake. Bwalo la limilandu likhoza kulamula mkazi kapena mwamuna kuti adzipeleka ndalama
kwa mzake mogwilizana ndi kapezedwe xx xxxxxxx kapena kakhalidwe ka mwamunayo kapena mkaziyo. Bwalo lamilandu limayenela kukhutitsidwa kuti mkazi kapena mwamuna akhoza kukwanitsa kupeleka ndalama za chisamalilo kapena zachithandizo zimene zalamulidwa kuti zizipelekedwe.
(b) Bwalo lamilandu likhozanso kulamula kuti ndalama za chisamalilo kapena zachithandizo zipelekedwe mwathunthu pa kamodzi kapena moduladula popeleka pa mwezi uli onse kapena pa sabata lililonse mpakana pamene mwamunayo kapena mkaziyo adzamwalile.
(c ) Bwalo la milandu lili ndi mphamvu zolamula mwamuna kapena mkazi kuti asiye kupeleka ndalama za chisamalilo ngati mkazi kapena mwamuna akulephela kupeleka ndalamazo pa zifukwa zomveka bwino. Bwalo la milandu likhozanso kulamula kuti kapelekedwe ka kandalama kangoyimitsidwa xxxx mwakanthawi kuti kadzayambilenso pa tsogolo kapenanso kuti ndalama zoyenela kupelekedwa zichepetsedwe ndi cholinga chakuti mkazi kapena mwamuna akwanitse kumalipila.
(d ) Polamula kapelekedwe ka chisamalilo kwa mkazi kapena mwamuna, bwalo lamilandu lidzawonetsetsa xxxx xxx awo asavutike.
(e ) Bwalo la milandu likhozanso kulamula mkazi kapena mwamuna kuti adzipeleka thandizo la katundu wofunikila pa moyo wa munthu xxxxx xxxx, zovala, kapena zakudya m’malo mopeleka ndalama,.
8.1 Nyumba yokhala mkazi kapena mwamuna ukwati ukathetsedwa
(a) Bwalo la milandu linapatsidwa mphamvu zolamula kuti mkazi kapena mwamuna asatulutsidwe kapena kuti asaletsedwe kutengapo gawo m’nyumba imene amakhala pa nthawi ya ukwati wawo ngakhale pamene ukwatiwo wathetsedwa. Bwalo lamilandu likhoza kupeleka mlingo wa nthawi imene mkaziyo kapena mwamunayo angapitilize kumakhalabe m’nyumbayo kuchokela pamene ukwati watha; komanso
(b) Bwalo lamilandu likhoza kulamula kuti mwamuna kapena mkazi apezele mzake nyumba yoyenelela kuti adzikhalamo ndi xxx xxx ngati nyumba imene amakhala pa nthawi ya
ukwati ndi ya mkazi yekha kapena mwamuna yekha amene angakhalemo ukwati ukatha chifukwa chakuti:
(i ) Nyumbayo ndi ya kuntchito kwa mwamuna kapena mkazi; kapena
(ii ) Nyumbayo inapatsidwa kwa mwamuna yekha kapena mkazi yekha kuchokera kwa xxxxxx xxx kapena achibale ake kapena munthu wina aliyense ; kapena
(iii) Nyumbayo ndi ya makolo kapena achibale amwamuna kapena mkazi
(c) Polamula kuti mwamuna kapena mkazi apezele mzake nyumba yoti adzikhalamo ukwati utatha, bwalo la milandu likuyenela kulingalila mfundo izi:
(i ) Ndalama kapena xxxxx xxxxxxx mwamuna kapena mkazi alinazo;
(ii ) Zosowa pa moyo wa tsiku ndi tsiku za mwamuna kapena mkazi ndi xxx xxx zimene ziyenela kupelekedwa;
(iii) Umoyo ndi ubwino was mwamuna kapena mkazi ndi xxx;
(iv) Khalidwe la mwamuna ndi mkazi kwa mzake ;
(v) Zaka zimene mwamuna ndi mkazi anakhalila pa ukwati wawo;
(vi) Ngati mwamuna ndi mkazi anali akukhala kale mosiyana, bwalo la lamilandu lidzalingalila nthawi kapena zaka zimene akhalila mosiyana.
9.0 Kasungidwe ndi Kasamalidwe ka xxx pamene ukwati watha
(a) Bwalo la milandu lili ndi mphavu zolamula za yemwe adzasunge kapena kukhala ndi xxx pamene ukwati watha. Chofunika kudziwa ndi chakuti mkazi ndi mwamuna akhoza kugwilizana za amene adzasunge kapena kukhala ndi xxx pamene ukwati wawo watha. Izi zikatele mkazi ndi mwamuna akuyenela kuwuza bwalo lamilandu limene likakhutila ndi mgwirizanowu lidzawutsimikiza ngati chilamulo cha bwalolo.
(b) Ngati bwalo lamilandu lapemphwedwa kuti ligamule za amene adzasunge ndi kukhala ndi xxx pamene ukwati watha, bwalolo liyenela kulingalila mfundo izi:
(i) Zimene zingapititse patsogolo ubwino wa umoyo wa mwana;
(ii) Zofuna ndi malingalilo a mwana zimene zidzawunikidwe potengela msinkhu ndi zaka za mwanayo komanso malo amane anafotokozela zofuna zakezo;
(iv) Makhalidwe a mwamuna kapena mkazi pakasamalidwe ndi kaleledwe ka mwanayo pa nthawi ya ukwati wawo;
(c) Choyenela kudziwa ndi chakuti lamulo limazindikila kuti zonse zikakhala bwino, umoyo wa mwana umapita patsogolo komanso kusamalidwa bwino pamene mwanayo akukhala limodzi ndi omwe ali ndi udindo omusamalila pamodzi ndi azibale ake ndi cholinga chakuti adzikula ngati xxx a banja limodzi. Lamulo limazindikilanso kuti mwanayo akuyenelanso kukhala pa xxxxx wabwino ndi xxxxxx xxx ngakhale ukwati utatha. Izi zimathandizanso kuti mwanayo akule bwino mwachikondi.
(d) Polamula za amene adzasunge kapena kusamala mwana pamene ukwati xxxxx, bwalo lamilandu limalingalilanso za chiwopsezo pa moyo wa mwanayo chimene chingadze pokhudzana ndi kumalo kapena dela kumene osunga mwanayo adzikakhala naye komanso anthu amene azikakhala nawo.
Choyenela kudziwa ndi chakuti miyambo kapena chikhalidwe cha makolo kapena mtundu wakumene mkazi kapena mwamuna amachokela sidzizatengapo gawo pakagamulidwe xx xxxxx akuyenela kusunga mwana pamene ukwati watha.
10. Kagawidwe xx xxxxxxx pamene ukwati watha
Pamene ukwati watha, bwalo lamilandu lidzagawa katundu wa pa banjalo mwa chilungamo poganizila zosowa za mwamuna ndi mkazi potengela mfundo izi:
(a) Ndalama kapena chuma cha mkazi kapena mwamuna;
(b) Katundu wa mwamuna kapena mkazi;
(c) Zofunika za ndalama kwa mkazi kapena mwamuna pa moyo wawo;
(d) Ma udindo a mkazi kapena mwamuna;
(e) Umoyo umene mkazi ndi mwamuna amakhala pa nthawi ya ukwati wawo;
(f) Zaka za mwamuna kapena mkazi komanso umoyo wawo; kapenanso
(g) Chithandizo kapena chisamalilo chosiyanasiyana chimene mwamuna kapena mkazi amapeleka pakasamalidwe ka pakhomo pa nthawi ya ukwati wawo
Izi zikutanthauza kuti katundu wa pa banja akhoza kugawidwanso kwa mkazi kapena mwamuna amene sanalembedwe ntchito kapena amene samapanga bizinesi ina iliyonse yobweletsa ndalama pakhomo.Izi zili chomwecho chifukwa chakuti lamulo limazindikila kuti ntchito zimene mkazi kapena mwamuna amagwila pakhomo xxxxx kusamala xxx, kuphika, kuchapa ndi zofunika ndipo ndi za phindu ngati ndalama ndipo ziyenela kulingalilidwa pakagawidwe xx xxxxx cha xx xxxxx pamene ukwati watha.
11. Kusokoneza ukwati kwa anthu xxxxx
Lamulo limazindikila kuti pali anthu xxxxxx xxxxx angathe kusokoneza ukwati wa anzawo chifukwa cha ndalama, kapena poti ndi ankhoswe a ukwatiwo, kapena popeza kuti ndi chibale kapena amzake a mwamuna kapena mkazi wa pa banja. Pofuna kuthana ndi mkhalidwe osokoneza ma ukwati kuchokela kwa achibale, lamulo likufotokoza kuti munthu amene ali wa chibale wa mwamuna kapena wa mkazi amene mm’malankhulidwe kapena m’machitidwe ake wapanga chimodzi mwazinthu zimene titchulezi ndekuti wapalamula mlandu umene chilango chake ndikulipila chindapusa cha ndalama zokwana K100,000 ndi kukaseweza kundende kwa chaka chimodzi. Zochita ndi zolankhula zimene achibale akuletsedwa ndi izi:
(a) Zochita kapena zolankhula zimene zingapangitse kuti ukwati wa a chibale uwonongeke;
(b) Zochita kapena zolankhula zolimbikitsa khalidwe la loyipa la mkazi kapena la mwamuna limene lingasokoneze ukwati wawo;
(c) Zochita kapena zolankhula zimene zingapangitse mwamuna kapena mkazi kuti asiye kupeleka chisamalilo kwa mzake pa ukwatiwo;
(d ) Zochita kapena zolankhula zimene m’njila ina iliyonse zingapangitse kuti ukwati usokonekere.
Kupatula kupeleka chilango chokaseweza kundende kapena kulipila chindapusa, bwalo la milandu likhozanso kupeleka chilamulo choletsa wachibale amene Zochita ndi zolankhula zake zikusokoneza ukwati kapena zimene zingasokoneze ukwati kuti asiye zolankhulazo ndi machitidwe oletsedwawo. Bwalo lamilandu likhozanso kulamula kapasuleyi kuti apeleke ndalama zomupepesa mkazi kapena mwamuna amene ukwati wawo akuwusokoneza
12.0 Udindo opeleka chisamalilo kwa mkazi amene ali ndi pa thupi koma osakwatiwa
Lamulo likupeleka udindo kwa munthu amene wapeleka pa thupi kwa mkazi ngakhale asanakwatilane naye kuti adzipeleka chisamalilo kwa mkaziyo pa nthawi xxxxx xxx woyembekezela. Lamuloli linakhazikitsidwa ndi cholinga chofuna kuthana ndi mkhalidwe wa amuna amene amangopeleka pa thupi kwa mkazi ndi kumusiya yekha kuti adzivutika popanda kupeleka chisamalilo chilichonse pamene mkaziyo ali oyembekezela.
(a) Mwamuna akapeleka pa thupi kwa mkazi wosakwatilana naye ndipo akuvomeleza kuti pathupipo anapeleka ndi iye akuyenela kupeleka chithandizo kapena chisamalilo kwa mkaziyo mpakana mwana atabadwa. Powonjezela apo, mwamunayo akuyenelanso kupeleka ndalama zimene mkazi wagwilitsa ntchito pobeleka mwana kuchipatala. Udindo umenewu umapelekedwanso kwa mwamuna amene akukana kuti si iye anapeleka pathupi koma bwalo la milandu lakhutitsidwa kuti anapeleka pathupipo ndi iyeyo.
(b) Mzimayi oyembekezela koma osakwatiwa ali ndi ufulu okapempha bwalo la milandu kuti lilamule mwamuna amene anapeleka pa thupi kuti ayambe kupeleka chisamalilo kwa
mkaziyo pa nthawi xxxxx xxx oyembekezela. Choyenela kudziwa ndi chakuti, makolo kapena achibale a mkazi oyembekezelayo ali ndi ufulu komanso udindo okapempha bwalo la milandu, mmalo mwa mkaziyo kuti mwamuna amene anapeleka pathupi ayambe kupeleka chisamalilo kapena chithandizo kwa mkaziyo.
(c ) Ngati mwamuna amene anapeleka pa thupi ndi wa zaka zakubadwa zochepela 18, udindo opeleka chisamalilo ndi chithandizo kwa mkazi oyembekezela udzapelekedwa kwa makolo a mwamunayo kapena amene akumulela mwamunayo mpakana pamene mwamunayo wakwanitsa za zakubadwa zokwana 18 kapena ngati wafika podziyimila payekha..
Lamulo latsopano la ma ukwati, mabanja ndi ma xxxxx ndi kuthetsa ma ukwati ndi lofunikila kwambili poteteza ndi kulimbikitsa ma ufulu ndi ma udindo a mwamuna ndi mkazi pa banja, xxx apabanja komanso mkazi amene wapatsidwa pathupi koma osakwatiwa. Onse owelenga lamulo latsopanoli akuyenela kufalitsa za uthenga wa bwino wa lamuloli ndi kulimbikitsa
anzawo kuti awalengenso za lamuloli.